Song Lyrics Search Engine

Lyrics  »  National Anthem lyrics  » 

malawi native anthem text lyrics

national anthem
Artist: national anthem
Song: malawi native anthem text
1.
Mlungu dalitsani Malawi,
Mumsunge m'mtendere.
Gonjetsani adani onse,
Njala, nthenda, nsanje.
Lunzitsani mitima yathu,
Kuti tisaope.
Mdalitse Mtsogo leri na fe,
Ndi Mai Malawi.
2.
Malawi ndziko lokongola,
La chonde ndi ufulu,
Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri,
Ndithudi tadala.
Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
N'mphatso zaulere.
Nkhalango, madambo abwino.
Ngwokoma Malawi.
3.
O! Ufulu tigwirizane,
Kukweza Malawi.
Ndi chikondi, khama, kumvera,
Timutumikire.
Pa nkhondo nkana pa mtendere,
Cholinga n'chimodzi.
Mai, bambo, tidzipereke,
Pokweza Malawi.
Sent by Carlos André Pereira da Silva Branco
national anthem
malawi native anthem text lyrics
by national anthem lyrics
duran duran
pretty ones lyrics
by duran duran lyrics
cancerslug
endless lyrics
by cancerslug lyrics
The Crüxshadows
sophia lyrics
by The Crüxshadows lyrics
three dog night
night in the city lyrics
by three dog night lyrics
beenie man
grindacologist lyrics
by beenie man lyrics
Latest Lyrics Additions: Hey Zeus the Dungeon / Snake In The Grass / Homies / G Check / Fuck The Club Up / Bricksquad / San Antonio Baby / Two Houses / To Me / One Less / Broken Girl / Hit the Parking Lot / Troubled World Pt.2 / Party / I Still / Everyday Struggle / Change / Can't Stay Away / The Perfect Space / I And Love And You